Mateyu 1:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo zonsezi zinakhala kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Ambuye mwa mneneri, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo zonsezi zinakhala kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Ambuye mwa mneneri, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Zonsezi zidaatero kuti zipherezere zimene Ambuye adaalankhulitsa mneneri kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Zonsezi zinachitika kukwaniritsa zimene Ambuye ananena mwa mneneri kuti, Onani mutuwo |