Mateyu 1:16 - Buku Lopatulika16 ndi Yakobo anabala Yosefe, mwamuna wake wa Maria, amene Yesu, wotchedwa Khristu, anabadwa mwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 ndi Yakobo anabala Yosefe, mwamuna wake wa Maria, amene Yesu, wotchedwa Khristu, anabadwa mwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Yakobe adabereka Yosefe, mwamuna wa Maria. Mariayu adabala Yesu, wotchedwa Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yakobo anabereka Yosefe, mwamuna wa Mariya. Mariyayu ndiye anabereka Yesu wotchedwa Khristu. Onani mutuwo |