Masalimo 94:1 - Buku Lopatulika1 Mulungu wakubwezera chilango, Yehova, Mulungu wakubwezera chilango, muoneke wowala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mulungu wakubwezera chilango, Yehova, Mulungu wakubwezera chilango, muoneke wowala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta, ndinu Mulungu wolipsira, Inu Mulungu wolanga, dziwonetseni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova, ndinu Mulungu wobwezera chilango, Inu Mulungu amene mumabwezera chilango, wonetsani kuwala kwanu. Onani mutuwo |