Masalimo 78:57 - Buku Lopatulika57 koma anabwerera m'mbuyo, nachita zosakhulupirika monga makolo ao, anapatuka ngati uta wolenda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 koma anabwerera m'mbuyo, nachita zosakhulupirika monga makolo ao, anapatuka ngati uta wolenda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 koma iwo adakhala okanika ndi osakhulupirika monga makolo ao. Adapotoka ngati uta wosakhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Anakhala okanika ndi osakhulupirika monga makolo awo, anapotoka monga uta wosakhulupirika. Onani mutuwo |