Masalimo 78:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anayesa Mulungu mumtima mwao ndi kupempha chakudya monga mwa kulakalaka kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anayesa Mulungu mumtima mwao ndi kupempha chakudya monga mwa kulakalaka kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Iwo adayesa Mulungu m'mitima mwao, pomuumiriza kuti aŵapatse chakudya chimene ankakhumba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ananyoza Mulungu mwadala pomuwumiriza kuti awapatse chakudya chimene anachilakalaka. Onani mutuwo |