Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 139:15 - Buku Lopatulika

15 Thupi langa silinabisikire Inu popangidwa ine mobisika, poombedwa ine monga m'munsi mwake mwa dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Thupi langa silinabisikira Inu popangidwa ine mobisika, poombedwa ine monga m'munsi mwake mwa dziko lapansi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Mapangidwe anga sadabisike pamaso panu pamene ndinkapangidwa mwachinsinsi, pamene ndinkaumbidwa mwaluso m'mimba mwa amai anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Mapangidwe anga sanabisike pamaso panu pamene ndimapangidwa mʼmalo achinsinsi, pamene ndinkawumbidwa mwaluso mʼmimba ya amayi anga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 139:15
7 Mawu Ofanana  

Pakuti Inu munalenga impso zanga; munandiumba ndisanabadwe ine.


Koma iwo amene afuna moyo wanga kuti auononge, adzalowa m'munsi mwake mwa dziko.


ndipo ana oyamba a m'dziko la Ejipito adzafa, kuyambira mwana woyamba wa Farao wokhala pa mpando wachifumu wake, kufikira mwana woyamba wa mdzakazi wokhala pa miyala yopera; ndi ana onse oyamba a zoweta.


Monga sudziwa njira ya mphepo, ngakhale makulidwe a mafupa m'mimba ya mkazi ali ndi pakati; momwemo sudziwa ntchito za Mulungu amene achita zonse.


Ndisanakulenge iwe m'mimba ndinakudziwa, ndipo usanabadwe ndinakupatula iwe; ndinakuika kuti ukhale mneneri wa mitundu ya anthu.


Koma ichi, chakuti, Anakwera, nchiyani nanga koma kuti anatsikiranso ku madera a kunsi kwa dziko?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa