Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 119:168 - Buku Lopatulika

168 Ndinasamalira malangizo anu ndi mboni zanu; popeza njira zanga zonse zili pamaso panu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

168 Ndinasamalira malangizo anu ndi mboni zanu; popeza njira zanga zonse zili pamaso panu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

168 Ndimatsata malamulo anu ndi malangizo anu, pakuti makhalidwe anga onse mukuŵaona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

168 Ndimamvera malangizo anu ndi umboni wanu, pakuti njira zanga zonse ndi zodziwika pamaso panu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:168
8 Mawu Ofanana  

Pakuti maso ake ali panjira ya munthu aliyense, napenya moponda mwake monse.


Muyesa popita ine ndi pogona ine, ndi njira zanga zonse muzolowerana nazo.


mitsinje iombe m'manja; mapiri afuule pamodzi mokondwera.


Pakuti njira za munthu zili pamaso pa Yehova, asinkhasinkha za mayendedwe ake onse.


Kodi munthu angathe kubisala mobisika kuti ndisamuone iye? Ati Yehova. Kodi Ine sindidzala kumwamba ndi dziko lapansi? Ati Yehova.


Ndipo palibe cholembedwa chosaonekera pamaso pake, koma zonse zikhala za pambalambanda ndi zovundukuka pamaso pake pa Iye amene tichita naye.


Ndipo ndidzaononga ana ake ndi imfa; ndipo idzazindikira Mipingo yonse kuti Ine ndine Iye amene ayesa impso ndi mitima; ndipo ndidzaninkha kwa yense wa inu monga mwa ntchito zanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa