Masalimo 103:5 - Buku Lopatulika5 Amene akhutitsa m'kamwa mwako ndi zabwino; nabweza ubwana wako unge mphungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Amene akhutitsa m'kamwa mwako ndi zabwino; nabweza ubwana wako unge mphungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndiye amene amakupatsa zabwino nthaŵi zonse za moyo wako, choncho umakhalabe wa mphamvu zatsopano ngati mphungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino, kotero kuti umakhala wamphamvu zatsopano ngati mphungu. Onani mutuwo |