Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 9:34 - Buku Lopatulika

34 Koma iwo anakhala chete; pakuti anatsutsana wina ndi mnzake panjira, kuti, wamkulu ndani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Koma iwo anakhala chete; pakuti anatsutsana wina ndi mnzake panjira, kuti, wamkulu ndani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Ophunzirawo adangoti chete. Ndiye kuti zimene ankatsutsana panjirapo zinali zakuti wamkulu ndani pakati pao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Koma anakhala chete chifukwa ali mʼnjira amatsutsana za kuti wamkulu kuposa onse ndani.

Onani mutuwo Koperani




Marko 9:34
10 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anafunsana wina ndi mnzake, nati, Sitinatenge mikate.


Mchere uli wabwino; koma ngati mchere unasukuluka, mudzaukoleretsa ndi chiyani? Khalani nao mchere mwa inu nokha, ndipo khalani ndi mtendere wina ndi mnzake.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


osati monga ochita ufumu pa iwo a udindo wanu, koma okhala zitsanzo za gululo.


Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkulu wa iwo, satilandira ife.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa