Marko 9:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ananena nao, Ndithu ndinena ndi inu kuti, Alipo ena akuimirira pano, amene sadzalawa imfa konse, kufikira akaona Ufumu wa Mulungu utadza ndi mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yesu adaŵauzanso kuti, “Ndithu ndikunenetsa kuti alipo ena pompano omwe sadzafa asanaone Ufumu wa Mulungu utafika ndi mphamvu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndipo anawawuza kuti, “Zoonadi, ndikuwuzani kuti ena amene ayimirira pano sadzafa asanaone ufumu wa Mulungu ukubwera mwa mphamvu.” Onani mutuwo |