Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 8:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anatsutsana wina ndi mnzake, nanena kuti, Tilibe mikate.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anatsutsana wina ndi mnzake, nanena kuti, Tilibe mikate.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Apo ophunzirawo adayamba kukambirana nkumati, “Akuterotu chifukwa tilibe buledi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iwo anakambirana wina ndi mnzake ndipo anati, “Ndi chifukwa choti tilibe buledi.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 8:16
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawalamula, nanena, Yang'anirani, penyani kuti mupewe chotupitsa mkate cha Afarisi, ndi chotupitsa mkate cha Herode.


Ndipo Yesu pamene anazindikira, ananena nao, Bwanji mutsutsana chifukwa mulibe mkate? Kodi kufikira tsopano simuzindikira, nisimudziwitsa? Kodi muli nayo mitima yanu youma?


Ndipo anatsutsana mwa okha, nanena, Ngati tinena uchokera Kumwamba; adzati, Simunamkhulupirire chifukwa ninji?


Ndipo anayamba kutsutsana kuti wamkulu mwa iwo ndani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa