Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 4:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Mbeu zofesedwa pa zitsamba za minga zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;

Onani mutuwo Koperani




Marko 4:18
6 Mawu Ofanana  

Pakuti Yehova atero kwa anthu a Yuda ndi kwa Yerusalemu, Limani masala anu, musabzale paminga.


Ndipo iye amene afesedwa kuminga, uyu ndiye wakumva mau; ndipo kulabadira kwa dziko lapansi, ndi chinyengo cha chuma chitsamwitsa mau, ndipo akhala wopanda chipatso.


ndipo alibe mizu mwa iwo okha, koma akhala kanthawi; pamenepo pakudza masautso kapena mazunzo chifukwa cha mau, pomwepo akhumudwa.


ndipo malabadiro a dziko lapansi, ndi chinyengo cha chuma, ndi kulakalaka kwa zinthu zina, zilowamo, zitsamwitsa mau, ndipo akhala opanda chipatso.


Ndipo zina zinagwa paminga, ndipo minga inakula, nkuzitsamwitsa, ndipo sizinabale zipatso.


Ndipo zija zinagwa kumingazi, ndiwo amene adamva, ndipo m'kupita kwao atsamwitsidwa ndi nkhawa, ndi chuma, ndi zokondweretsa za moyo, ndipo sakhwimitsa zipatso zamphumphu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa