Marko 4:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo ena ndiwo akufesedwa kuminga; iwo ndiwo amene adamva mau, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mbeu zofesedwa pa zitsamba za minga zija zikutanthauza anthu amene amaŵamva mau a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu; Onani mutuwo |