Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 3:30 - Buku Lopatulika

30 pakuti adanena, Ali ndi mzimu wonyansa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 pakuti adanena, Ali ndi mzimu wonyansa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Yesu adalankhula zimenezi poona kuti anthu aja ankanena kuti, “Wagwidwa ndi mzimu woipa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ananena izi chifukwa anati, “Ali ndi mzimu woyipa.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 3:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo alembi amene adatsika ku Yerusalemu ananena kuti, Ali naye Belezebulu, ndipo, Ndi mkulu wao wa ziwanda atulutsa ziwanda.


koma aliyense adzachitira Mzimu Woyera mwano alibe kukhululukidwa nthawi yonse, koma anapalamuladi tchimo losatha;


Ndipo anadza amake ndi abale ake; naima kunja, namtumira uthenga kumuitana.


Koma ambiri mwa iwo ananena, Ali ndi chiwanda, nachita misala; mukumva Iye bwanji?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa