Marko 15:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo anayankha, nanena naye, Mwatero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo anayankha, nanena naye, Mwatero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pilatoyo adafunsa Yesu kuti, “Kodi iwe, ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Yesu adamuyankha kuti, “Mwanena nokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pilato anafunsa kuti, “Kodi Iwe ndi Mfumu ya Ayuda?” Yesu anayankha kuti, “Mwatero ndinu.” Onani mutuwo |