Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 15:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo anayankha, nanena naye, Mwatero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo Pilato anamfunsa Iye, Kodi ndiwe mfumu ya Ayuda? Ndipo anayankha, nanena naye, Mwatero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Pilatoyo adafunsa Yesu kuti, “Kodi iwe, ndiwe Mfumu ya Ayuda?” Yesu adamuyankha kuti, “Mwanena nokha.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Pilato anafunsa kuti, “Kodi Iwe ndi Mfumu ya Ayuda?” Yesu anayankha kuti, “Mwatero ndinu.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 15:2
11 Mawu Ofanana  

nati, Ali kuti amene anabadwa mfumu ya Ayuda? Chifukwa tinaona nyenyezi yake kum'mawa, ndipo tinadzera kudzamlambira Iye.


Ndipo Pilato anawayankhanso, nati kwa iwo, Pamenepo ndidzachita chiyani ndi Iye amene mumtchula mfumu ya Ayuda?


Ndipo anayamba kumlankhula Iye, kuti, Tikuoneni, mfumu ya Ayuda!


Ndipo lembo la mlandu wake linalembedwa pamwamba, MFUMU YA AYUDA.


Ndipo ansembe aakulu anamnenera Iye zinthu zambiri.


Ndipo Pilato anawayankha, nanena nao, Kodi mufuna kuti ndikumasulireni mfumu ya Ayuda?


Ndikulamulira pamaso pa Mulungu, wozipatsa zinthu zonse moyo, ndi Khristu Yesu, amene anachitira umboni chivomerezo chabwino kwa Pontio Pilato;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa