Marko 14:8 - Buku Lopatulika8 Iye wachita chimene wakhoza; anandidzozeratu thupi langa ku kuikidwa m'manda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Iye wachita chimene wakhoza; anandidzozeratu thupi langa ku kuikidwa m'manda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Iyeyu wachita zimene akadatha kuchita. Wadzozeratu thupi langa ndi mafuta onunkhira, kuti alikonzeretu lisanaikidwe m'manda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Wachita zimene akanatha. Wathira mafuta onunkhira pa thupi langa nthawi isanakwane kukonzekera kuyikidwa kwanga mʼmanda. Onani mutuwo |