Marko 14:6 - Buku Lopatulika6 Koma Yesu anati, Mlekeni, mumvutiranji? Wandichitira Ine ntchito yabwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma Yesu anati, Mlekeni, mumvutiranji? Wandichitira Ine ntchito yabwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma Yesu adati, “Mlekeni maiyu, mukumuvutiranji kodi? Zimenetu wandichitira iyeyuzi nzabwino kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yesu anati, “Musiyeni, chifukwa chiyani mukumuvutitsa? Wandichitira Ine chinthu chabwino. Onani mutuwo |