Marko 14:2 - Buku Lopatulika2 pakuti anati, Pachikondwerero ai, kuti pangakhale phokoso la anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 pakuti anati, Pachikondwerero ai, kuti pangakhale phokoso la anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Koma ankati, “Zimenezi tisadzachite pa nthaŵi ya chikondwerero ai, pangadzachitike chipolowe pakati pa anthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iwo anati, “Koma osati nthawi yaphwando, chifukwa anthu angachite chiwawa.” Onani mutuwo |