Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 1:43 - Buku Lopatulika

43 Ndipo anamuuzitsa, namtulutsa pomwepo,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Ndipo anamuuzitsa, namtulutsa pomwepo,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Tsono Yesu adamlamula kuti apite, namuuza mau amphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Nthawi yomweyo Yesu anamuwuza kuti apite koma anamuchenjeza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Marko 1:43
7 Mawu Ofanana  

Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo pomwepo khate linamchoka, ndipo anakonzedwa.


nanena naye, Ona, usati unene kanthu kwa munthu aliyense: koma muka, ukadzionetse kwa wansembe, nupereke pa makonzedwe ako zimene adalamulira Mose, zikhale mboni kwa iwo.


Ndipo anailimbitsira mau kuti isamuulule Iye.


Ndipo anawalamulira kwambiri kuti asadziwe ichi munthu mmodzi, nawauza kuti ampatse iye kudya.


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.


Ndipo atate wake ndi amake anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu aliyense chimene chinachitika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa