Malaki 2:9 - Buku Lopatulika9 Chifukwa chake Inenso ndakuikani onyozeka ndi ochepseka kwa anthu onse, popeza simunasunge njira zanga, koma munaweruza mwankhope pochita chilamulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chifukwa chake Inenso ndakuikani onyozeka ndi ochepseka kwa anthu onse, popeza simunasunga njira zanga, koma munaweruza mwankhope pochita chilamulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nchifukwa chake Inenso ndakusandutsani onyozeka ndi achabechabe pamaso pa anthu, popeza kuti simudatsate njira zanga, ndipo mwakhala mukukondera poweruza milandu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Choncho Ine ndachititsa kuti munyozedwe ndi kuchititsidwa manyazi pamaso pa anthu onse, chifukwa simunatsate njira zanga koma mwakhala mukuonetsa kukondera pa nkhani za malamulo.” Onani mutuwo |