Malaki 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo tsopano, mupepeze Mulungu, kuti atichitire chifundo; ichicho chichokera kwa inu; kodi Iye adzavomereza ena a inu? Ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo tsopano, mupepeze Mulungu, kuti atichitire chifundo; ichicho chichokera kwa inu; kodi Iye adzavomereza ena a inu? Ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsopano tayesani kupempha Mulungu kuti akuchitireni chifundo. Ndi mphatso zotere m'manja mwanu, kodi angakomere mtima aliyense mwa inu? Tsono Chauta Wamphamvuzonse akupitiriza kunena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Tsopano tayesani kupempha Mulungu kuti akuchitireni chifundo. Kodi ndi zopereka zotere mʼmanja mwanu, Iye angakulandireni?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |