Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Malaki 1:1 - Buku Lopatulika

1 Katundu wa mau a Yehova wa kwa Israele mwa Malaki.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Katundu wa mau a Yehova wa kwa Israele mwa Malaki.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Nawu uthenga wa Chauta kwa Aisraele kudzera mwa Malaki.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Uthenga: Mawu a Yehova kwa Israeli kudzera mwa Malaki.

Onani mutuwo Koperani




Malaki 1:1
9 Mawu Ofanana  

Katundu wa Babiloni, amene anamuona Yesaya mwana wa Amozi.


Ndipo pamene anthu awa, kapena mneneri, kapena wansembe, adzakufunsa iwe, kuti, Katundu wa Yehova ndi chiyani? Pamenepo uziti kwa iwo, Katundu wanji? Ndidzakuchotsani inu, ati Yehova.


Katundu wa Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi.


Katundu adamuona mneneri Habakuku


Chaka chachiwiri cha mfumu Dariusi, mwezi wachisanu ndi chimodzi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri kwa Zerubabele mwana wa Sealatiele, chiwanga cha Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kuti,


Mwezi wachisanu ndi chiwiri, tsiku la makumi awiri ndi chimodzi la mweziwo, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri, ndi kuti,


Katundu wa mau a Yehova wakunena Israele. Atero Yehova, wakuyala miyamba, ndi kuika maziko a dziko lapansi, ndi kulenga mzimu wa munthu m'kati mwake;


Katundu wa mau a Yehova padziko la Hadaraki, ndipo Damasiko adzakhala popumula pake; pakuti Yehova apenyerera anthu monga apenyerera mafuko onse a Israele;


Yuda wachita monyenga, ndi mu Israele ndi mu Yerusalemu mwachitika chonyansa; pakuti Yuda waipsa chipatuliko cha Yehova chimene achikonda, nakwatira mwana wamkazi wa mulungu wachilendo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa