Malaki 1:1 - Buku Lopatulika1 Katundu wa mau a Yehova wa kwa Israele mwa Malaki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Katundu wa mau a Yehova wa kwa Israele mwa Malaki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nawu uthenga wa Chauta kwa Aisraele kudzera mwa Malaki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uthenga: Mawu a Yehova kwa Israeli kudzera mwa Malaki. Onani mutuwo |