Machitidwe a Atumwi 8:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Saulo anapasula Mpingo, nalowa nyumba ndi nyumba, nakokamo amuna ndi akazi, nawaika m'ndende. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Saulo anapasula Mpingo, nalowa nyumba ndi nyumba, nakokamo amuna ndi akazi, nawaika m'ndende. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma Saulo uja ankapasula Mpingo. Ankaloŵa m'nyumba za anthu, namagwira amuna ndi akazi omwe, nkumaŵaponya m'ndende. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma Saulo anayamba kuwononga mpingo. Amapita nyumba ndi nyumba, ndipo amagwira amuna ndi amayi ndi kukawatsekera ku ndende. Onani mutuwo |