Machitidwe a Atumwi 4:30 - Buku Lopatulika30 m'mene mutambasula dzanja lanu kukachiritsa; ndi kuti zizindikiro ndi zozizwa zichitidwe mwa dzina la Mwana wanu wopatulika Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 m'mene mutambasula dzanja lanu kukachiritsa; ndi kuti zizindikiro ndi zozizwa zichitidwe mwa dzina la Mwana wanu wopatulika Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Tambalitsani dzanja lanu kuti anthu achire, ndipo pachitike zizindikiro ndi zozizwitsa m'dzina la Mtumiki wanu wopatulika.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Tambasulani dzanja lanu kuchiritsa anthu ndipo kuti, zizindikiro zodabwitsa zichitike mʼdzina la mtumiki wanu woyera Yesu.” Onani mutuwo |