Machitidwe a Atumwi 3:1 - Buku Lopatulika1 Koma Petro ndi Yohane analikukwera kunka ku Kachisi pa ora lakupembedza, ndilo lachisanu ndi chinai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma Petro ndi Yohane analikukwera kunka ku Kachisi pa ora lakupembedza, ndilo lachisanu ndi chinai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku lina Petro ndi Yohane ankapita ku Nyumba ya Mulungu pa 3 koloko madzulo, nthaŵi ya mapemphero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsiku lina Petro ndi Yohane ankapita ku Nyumba ya Mulungu kukapemphera nthawi ya 3 koloko masana. Onani mutuwo |