Machitidwe a Atumwi 2:10 - Buku Lopatulika10 mu Frijiya, ndiponso mu Pamfiliya, mu Ejipito, ndi mbali za Libiya wa ku Kirene, ndi alendo ochokera ku Roma, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 m'Frijiya, ndiponso m'Pamfiliya, m'Ejipito, ndi mbali za Libiya wa ku Kirene, ndi alendo ochokera ku Roma, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 ku Frijiya ndi ku Pamfiliya, ku Ejipito, ndi ku madera a Libiya kufupi ndi ku Kirene, ena ndi alendo ochokera ku Roma, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 ku Frugiya ndi Pamfiliya, ku Igupto ndi ku madera a ku Libiya kufupi ndi ku Kurene; alendo ochokera ku Roma, Onani mutuwo |