Machitidwe a Atumwi 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo pakufika tsiku la Pentekoste, anali onse pamodzi pamalo amodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo pakufika tsiku la Pentekoste, anali onse pamodzi pa malo amodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene tsiku la chikondwerero cha Pentekoste lidafika, iwo onse anali pamodzi m'nyumba imodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Litafika tsiku la chikondwerero cha Pentekosite, onse anali pamodzi. Onani mutuwo |
Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;