Machitidwe a Atumwi 14:2 - Buku Lopatulika2 Koma Ayuda osamvera anautsa mitima ya Agriki kuti aipse abale athu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma Ayuda osamvera anautsa mitima ya Agriki kuti aipse abale athu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Koma Ayuda amene sadakhulupirire adautsa mitima ya akunjawo kuti adane ndi akhristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma Ayuda amene anakana kukhulupirira anawutsa anthu a mitundu ina nawononga maganizo awo kutsutsana ndi abale. Onani mutuwo |