Machitidwe a Atumwi 13:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pokhala ku Salami, analalikira mau a Mulungu m'masunagoge a Ayuda; ndipo anali nayenso Yohane mnyamata wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pokhala ku Salami, analalikira mau a Mulungu m'masunagoge a Ayuda; ndipo anali nayenso Yohane mnyamata wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Atafika ku mzinda wa Salami, adalalika mau a Mulungu m'nyumba zamapemphero za Ayuda. Analinso ndi Yohane womaŵathandiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamene anafika ku Salamisi, analalikira Mawu a Mulungu mʼMasunagoge a Ayuda. Iwo anali ndi Yohane monga wowatumikira. Onani mutuwo |