Machitidwe a Atumwi 13:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo, m'mene adasala chakudya ndi kupemphera ndi kuika manja pa iwo, anawatumiza amuke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo, m'mene adasala chakudya ndi kupemphera ndi kuika manja pa iwo, anawatumiza amuke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono atasala zakudya ndi kupemphera adaŵasanjika manja naŵatuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo atasala kudya ndi kupemphera anasanjika manja awo pa iwo nawatumiza. Onani mutuwo |