Machitidwe a Atumwi 11:1 - Buku Lopatulika1 Koma atumwi ndi abale akukhala mu Yudeya anamva kuti amitundunso adalandira mau a Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Koma atumwi ndi abale akukhala m'Yudeya anamva kuti amitundunso adalandira mau a Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Atumwi aja, ndiponso abale onse amene anali ku Yudeya, adamva kuti anthu a mitundu ina nawonso alandira mau a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Atumwi ndi abale a ku Yudeya konse anamva kuti anthu a mitundu ina analandiranso Mawu a Mulungu. Onani mutuwo |