Machitidwe a Atumwi 1:5 - Buku Lopatulika5 pakuti Yohane anabatizadi ndi madzi; koma inu mudzabatizidwa ndi Mzimu Woyera, asanapite masiku ambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 pakuti Yohane anabatizadi ndi madzi; koma inu mudzabatizidwa ndi Mzimu Woyera, asanapite masiku ambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pajatu Yohane ankabatiza ndi madzi, koma pasanapite masiku ambiri, inu mudzabatizidwa ndi Mzimu Woyera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pakuti Yohane anakubatizani ndi madzi, koma posachedwapa inu mudzabatizidwa ndi Mzimu Woyera.” Onani mutuwo |