Luka 9:47 - Buku Lopatulika47 Koma Yesu pakuona kutsutsana kwa mitima yao, anatenga kamwana, nakaimika pambali pake, nati kwa iwo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Koma Yesu pakuona kutsutsana kwa mitima yao, anatenga kamwana, nakaimika pambali pake, nati kwa iwo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Koma Yesu adaadziŵa zimene zinali kukhosi kwao. Tsono adatenga mwana, namukhazika pambali pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Yesu podziwa maganizo awo, anatenga kamwana nakayimika pambali pake. Onani mutuwo |