Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Yesu adalamula ophunzira ake kuti asauze munthu wina aliyense zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Yesu anawachenjeza kwambiri kuti asawuze wina aliyense za izi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:21
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo analamulira ophunzira kuti asauze munthu kuti Iye ndiye Khristu.


Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalamula iwo kuti, Musakauze munthu choonekacho, kufikira Mwana wa Munthu adadzauka kwa akufa.


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa