Luka 9:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Iye anawauzitsa iwo, nalamulira kuti asanene ichi kwa munthu aliyense; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yesu adalamula ophunzira ake kuti asauze munthu wina aliyense zimenezi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yesu anawachenjeza kwambiri kuti asawuze wina aliyense za izi. Onani mutuwo |