Luka 9:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anawatuma kukalalikira Ufumu wa Mulungu, ndi kuchiritsa anthu odwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anawatuma kukalalikira Ufumu wa Mulungu, ndi kuchiritsa anthu odwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adaŵatuma kuti akalalike za ufumu wa Mulungu, ndi kukachiritsa anthu odwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo Iye anawatumiza kukalalikira za ufumu wa Mulungu ndi kukachiritsa odwala. Onani mutuwo |