Luka 8:44 - Buku Lopatulika44 anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chovala chake; ndipo pomwepo nthenda yake inaleka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chovala chake; ndipo pomwepo nthenda yake inaleka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Iyeyu adafika cha kumbuyo kwa Yesu, nakhudza mphonje ya chovala chake, ndipodi nthaŵi yomweyo matenda a msambowo adaleka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Iye anafika kumbuyo kwake ndi kukhudza mothera mwa chovala chake, ndipo nthawi yomweyo magazi ake analeka kutuluka. Onani mutuwo |