Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo pamene khamu lalikulu la anthu linasonkhana, ndi anthu a kumidzi yonse anafika kwa Iye, anati mwa fanizo:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo pamene khamu lalikulu la anthu linasonkhana, ndi anthu a kumidzi yonse anafika kwa Iye, anati mwa fanizo:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Anthu ambirimbiri ochokera ku midzi yonse adasonkhana kumene kunali Yesu. Tsono Iye adaŵaphera fanizo. Adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Anthu ambiri ankasonkhana, ndipo pamene anthu ankabwera kwa Yesu kuchokera ku midzi, Iye anawawuza fanizo ili,

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:4
4 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo Yesu anatuluka m'nyumbamo, nakhala pansi m'mbali mwa nyanja.


Anatuluka wofesa kukafesa mbeu zake; ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira; ndipo zinapondedwa, ndi mbalame za m'mlengalenga zinatha kuzidya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa