Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo amene anaona anawauza iwo machiritsidwe ake a wogwidwa chiwandayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo amene anaona anawauza iwo machiritsidwe ake a wogwidwa chiwandayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Anzao amene adaaonerera zonse zikuchitika, adaŵasimbira m'mene munthu wamizimuyo adaamchiritsira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Amene anaona izi anawuza anthu mmene munthu wogwidwa ndi ziwandayo anachiritsidwira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:36
2 Mawu Ofanana  

Ndipo mbiri yake inabuka ku Siriya konse: ndipo anatengera kwa Iye onse akudwala, ogwidwa ndi nthenda ndi mazunzo a mitundumitundu, ndi ogwidwa ndi ziwanda, ndi akhunyu, ndi amanjenje; ndipo Iye anawachiritsa.


Ndipo anthu aunyinji onse a dziko la Agerasa loyandikira anamfunsa Iye achoke kwa iwo; chifukwa anagwidwa ndi mantha aakulu. Ndipo Iye analowa m'ngalawa, nabwerera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa