Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 6:36 - Buku Lopatulika

36 Khalani inu achifundo monga Atate wanu ali wachifundo. Ndipo musamaweruza, ndipo simudzaweruzidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Khalani inu achifundo monga Atate wanu ali wachifundo. Ndipo musamaweruza, ndipo simudzaweruzidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Monga Atate anu akumwamba ali achifundo, inunso mukhale achifundo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Khalani achifundo, monga momwe Atate anu ali achifundo.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 6:36
7 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake inu mukhale angwiro, monga Atate wanu wa Kumwamba ali wangwiro.


Koma takondanani nao adani anu, ndi kuwachitira zabwino, ndipo kongoletsani osayembekeza kanthu konse, ndipo mphotho yanu idzakhala yaikulu, ndipo inu mudzakhala ana a Wamkulukuluyo; chifukwa Iye achitira zokoma anthu osayamika ndi oipa.


Ndipo musawatsutsa, ndipo simudzamatsutsidwa. Khululukani, ndipo mudzakhululukidwa.


Chiwawo chonse, ndi kupsa mtima, ndi mkwiyo, ndi chiwawa, ndi mwano zichotsedwe kwa inu, ndiponso choipa chonse.


Koma nzeru yochokera kumwamba iyamba kukhala yoyera, nikhalanso yamtendere, yaulere, yomvera bwino, yodzala chifundo ndi zipatso zabwino, yopanda tsankho, yosadzikometsera pamaso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa