Luka 6:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo kutacha, anaitana ophunzira ake; nasankha mwa iwo khumi ndi awiri, amene anawatchanso dzina lao atumwi: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo kutacha, anaitana ophunzira ake; nasankha mwa iwo khumi ndi awiri, amene anawatchanso dzina lao atumwi: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kutacha adaitana ophunzira ake, nasankhapo khumi ndi aŵiri. Adaŵatcha “atumwi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kutacha, anayitana ophunzira ake ndipo anasankha khumi ndi awiri a iwo amene anawayika kukhala atumwi: Onani mutuwo |