Luka 6:11 - Buku Lopatulika11 Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma akuluakulu aja adakwiya kwambiri, nayamba kukambirana zoti achite naye Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma iwo anapsa mtima nayamba kukambirana wina ndi mnzake chomwe akanamuchitira Yesu. Onani mutuwo |