Luka 5:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo pamene Iye analeka kulankhula, anati kwa Simoni, Kankhira kwa kuya, nimuponye makoka anu kukasodza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo pamene Iye analeka kulankhula, anati kwa Simoni, Kankhira kwa kuya, nimuponye makoka anu kukasodza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Atatsiriza kulankhula, adauza Simoni kuti, “Sunthirani kozamako, muponye makoka anu kuti muphe nsomba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Atatha kuyankhula anati kwa Simoni, “Kankhirani kwa kuya ndipo muponye makhoka kuti mugwire nsomba.” Onani mutuwo |