Luka 5:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Iye anatambalitsa dzanja lake, namkhudza, nanena, Ndifuna, takonzeka. Ndipo pomwepo khate linachoka kwa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Iye anatambalitsa dzanja lake, namkhudza, nanena, Ndifuna, takonzeka. Ndipo pomwepo khate linachoka kwa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Yesu adatambalitsa dzanja nkumukhudza, nati, “Chabwino, ndikufuna, chira!” Pomwepo khate lake lija lidatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yesu anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo. Iye anati, “Ine ndikufuna, yeretsedwa!” Ndipo nthawi yomweyo khate lake linachoka. Onani mutuwo |