Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:30 - Buku Lopatulika

30 Koma Iye anapyola pakati pao, nachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Koma Iye anapyola pakati pao, nachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 koma Iye adangodzadutsa pakati pao, nkumapita.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Koma Iye anangoyenda pakati pa gulu la anthulo nachokapo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anatsika nadza ku Kapernao, ndiwo mzinda wa ku Galileya. Ndipo analikuwaphunzitsa iwo pa Sabata; ndipo anadabwa ndi chiphunzitso chake;


Anafunanso kumgwira Iye; ndipo anapulumuka m'dzanja lao.


Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi.


Koma kutacha, panali phokoso lalikulu mwa asilikali, Petro wamuka kuti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa