Luka 4:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anapereka kwa Iye buku la Yesaya mneneri. Ndipo m'mene Iye adafunyulula bukulo, anapeza pomwe panalembedwa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anapereka kwa Iye buku la Yesaya mneneri. Ndipo m'mene Iye adafunyulula bukulo, anapeza pomwe panalembedwa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Adampatsa buku la mneneri Yesaya. Tsono Iye adafutukula bukulo, napeza pamene padalembedwa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Anamupatsa buku la mneneri Yesaya. Atalitsekula, anapeza pamalo pamene panalembedwa kuti, Onani mutuwo |