Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:9 - Buku Lopatulika

9 nabwera kuchokera kumanda, nafotokozera zonse khumi ndi mmodziwo, ndi otsala onse omwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 nabwera kuchokera kumanda, nafotokozera zonse khumi ndi mmodziwo, ndi otsala onse omwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 ndipo atabwerako kumanda kuja, adasimbira zonsezo ophunzira khumi ndi mmodzi aja, ndi anthu ena onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Atabwerera kuchokera ku mandako, anafotokoza zinthu zonse kwa khumi ndi mmodziwo ndi kwa ena onse.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:9
6 Mawu Ofanana  

Iyeyu anapita kuwauza iwo amene ankakhala naye, ali ndi chisoni ndi kulira misozi.


Koma panali Maria wa Magadala, ndi Yohana, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi akazi ena pamodzi nao amene ananena izi kwa atumwiwo.


Ndipo anakumbukira mau ake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa