Luka 24:6 - Buku Lopatulika6 Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso mu Galileya, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso m'Galileya, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Sali muno ai, wauka. Kumbukirani zimene adaakuuzani akadali ku Galileya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye sali muno ayi. Wauka! Kumbukirani zimene anakuwuzani pamene anali nanu ku Galileya: Onani mutuwo |