Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:12 - Buku Lopatulika

12 Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zabafuta pazokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zoyera pa zokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Komabe Petro adanyamuka nathamangira ku manda. Adaŵeramiramo naona nsalu zamaliro zokha, kenaka nkubwerera kunyumba akudabwa ndi zimene zidaachitikazo.]

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Komabe Petro anayimirira ndi kuthamangira ku manda. Atasuzumira, anaona nsalu zimene anamukulungira zija zili pa zokha, ndipo iye anachoka, akudabwa ndi zimene zinachitikazo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:12
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo anatenga mtembo wa Yesu, nauzenenga ndi nsalu zabafuta pamodzi ndi zonunkhira, monga mwa maikidwe a maliro a Ayuda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa