Luka 23:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yesu adati, “Atate, muŵakhululukire anthuŵa, chifukwa sakudziŵa zimene akuchita.” Iwo aja adagaŵana zovala zake pakuchita maere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yesu anati, “Atate, akhululukireni, pakuti sakudziwa chimene akuchita.” Ndipo anagawana malaya ake mochita maere. Onani mutuwo |