Luka 21:10 - Buku Lopatulika10 Pamenepo ananena nao, Mtundu wa anthu udzaukira pa mtundu wina, ndipo ufumu pa ufumu wina: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pamenepo ananena nao, Mtundu wa anthu udzaukira pa mtundu wina, ndipo ufumu pa ufumu wina: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Yesu adaŵauzanso kuti, “Mitundu yosiyanasiyana idzaukirana, maiko osiyanasiyana adzamenyana nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kenaka anawawuza kuti, “Mtundu wa anthu udzawukirana ndi mtundu wina, ndi ufumu kuwukira ufumu wina. Onani mutuwo |