Luka 20:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ana a dziko lapansi akwatira nakwatiwa: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Yesu anati kwa iwo, Ana a dziko lapansi akwatira nakwatiwa: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Yesu adaŵayankha kuti, “Anthu okhala pansi pano amakwatira ndi kukwatiwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yesu anayankha kuti, “Anthu a mʼbado uno amakwatira ndi kukwatiwa. Onani mutuwo |